Promoting independent living . Kulimbikitsa kukhala ndi moyo wodziimila.

  • Home
  • Malawi
  • Dedza
  • Promoting independent living . Kulimbikitsa kukhala ndi moyo wodziimila.
20/03/2025

Kodi timanva bwanji pa imfa ya Yesu?

Ndizonvesa chisoni kwambili kuti nkhanza padzikoli zinayamba kalekale kufikila pano nkhaza zikupitililabe ndikutelo chifukwa tikawona ndimomwe dzikoli lili pano ariyese akadzuka ndi moyo kwatsiku limenelo akuyamika kumwamba 🙏

Yesu anazunzidwa momamukwapula zomwe zinali zopanda wulemu mpaka kumukoloweka chthu cholemela kuti aziyenda nacho kwinaku akukwapulidwa abale ndi imfa yowawa kuvulidwa zovala nkumakwapulidwa kumangidwa manja ndi zigwe zomwe zinali nkhaza kwaiyeyu

Zinalizovuta kuti iye athawe chifukwa anali kukhulupilila mulungu komanso zinali zolembedwa kale kuti adzapangidwa chipogwe padzikoli NDE nkhaza zimenezi panoso zilipo ndipo zilidzokolonse lapasi timatchula dzina la Yesu chifukwa iye anasonyeza kulimba mtima kunali kumuukila ndipodi athuwo anapangadi kufuna kwawo Yesu analimba mtima povomeleza pachimenechi

Zinalizonvesa chisoni kupachikidwa pantanda Mai ake akuwona (maria) ndipo anakhomedwa ali wamoyopantanda iye aliponpo anayankhula mawu omwe lelolino ndi chipulumutso cha athu a dziko lonse lapansi ndani mwaife angakhomedwe misomali nmanja onse awili mowatambasula kuphatikizapo miyendo koma nkukhalabe ndimoyo komanso nphanvu kukwanitsa kuyankhula? Ndani mwaife angalole kupeleka moyo wake kwamitumduyonse pofuna kubweletsa ntendele? Ndikukhulupilila sangapezeke yesu anapanga zonsezi yekha ndipo lelo ndichifukwa chake tikutansa ndi mawufulu oti wina anatikonzela kale

Tikuyenera kukhala achifundo nthawizonse powafunila azathu zabwino kapena kugwananawo zithu zomwe tilinanzo Yesu anasonyeza kulimba mtima mwachikhulupilo ndipodi athu analitu kulikita ngati simuthu nzawo ai samalemekezaso ai kodi pano sitimalemekeza atsongolele amaiko or anpingo? Timawalemekeza chifukwa ndi opatulika koma wufulu osewu anamenya ndi yesu podzipeleka yekha ku imfa

Awuzeni anebawo kuti ndinu opatulika chifukwa yesu anakufelani wufumu omwe mulinawowu anakumenyelani ndi Yesu kwaine ndimaphuzila zambili komanso ndimakhulupilila

19/03/2025

Moyo wapano ndi vala dzilimbe

19/03/2025

Kulapa ndinjila yokhazikitsa ntendele pamoyo wako.

Dziko lililonse timapita ndi passport popanda passport sungayende wulendo wabwino ndichimodzimodziso pomwe tikudikila kulowa wufumu wamulungu tikuyenera kulapa

Kulapa kulingati kudula passport yolowela mu ufumu wamulungu koma chonvetsa chisoni padzikolapasi sitimalemekeza komanso kusamala zomwe baibulo limaphuzitsa.

Apa pomwe tili ndimoyo tilingati tikudikila galimoto yotiititenge kupita kwinakwake zikufananaso kudikila wufumu wamulungu and galimoto simanyamuka isadadzaze ai ndipo oyendetsa amayesetsa idzaze kenako nkuyamba wulendo mulungu akudikila kuti titembenuke ntima kenako aweluze dzikoli ndagwilitsa ntchito zithu zomwe sizovuta kuzinvetsa komanso ndimomwe pano dziko kapena moyo wukuyendela zikumasonyezelatu kuti dzikoli likupita kumapeto chikufunika ndikumakhala okonzeka mwakulapa ndicholinga choti adzatipeze tili oyela mtima

Tidikilile mpaka minibasi idzaze tidikilile mpaka mulungu aweluze dzikoli koma tisafooke ndikudikila pakupanga zosayenela pamoyo wathu tingakhale palizambi zokhumudwitsa moyo wumadusa munzambili.

Ambuye akudaliseni makoma nonse🙏

19/03/2025

Mwadzuka bwanji konse komwe muliko?

18/03/2025

Amayi tsalani kumudzi npitandine ? Tiwone amene adapita ku Church 😁😁

18/03/2025

Ndine saylet Alex ndimachoka ku Dedza T/A kasumbu.

Ineyo ndimalimbikitsa achinyamata azanga kukhala ndi moyo wodziimila ,promoting independent , NDE ndikupenpha achinyamata azanga kundi tsatila pa page yanga pondilimbikitsa kuti ineso ndikulimbikitseni zomwe ndilinozo popanga like komanso comment

By [email protected]

18/03/2025

Koma fb isadzathe abale iyaaa pamakhala zosangalatsa zambili mudzangova hallelujah aaaa pa fb kutelo simachokapo ine 🤣🤣🤣🤣🤣

18/03/2025

Mulungu wanphanvu zonse ndiwamuyaya munalola kuti tibwele kuno kudzasaka ndikukupenpha kuti mupitilize kundiyang,nila pomwe ndikupitiliza kusaka zakuthupi ndikupenphaso asanjikileni dzanja lani lamanja awo sakupeza ntchito kuti apeze thandizo ndapenpha zonsezi kudzela mwa nkhilistu Yes amen🙏

17/03/2025

Pomwe tikugona tisaiwale nkupenphera🙏

17/03/2025

Chilango chamulungu sichimathawika koma chilango chamuthu chimathawika zomwe zikusonyeza kuti muthu aribe nphanvu yopasa muthu chilango mulungu ndiye tate wa ma tate

17/03/2025

Kwacha bwino kaya kumeneko kwacha bwanji?

15/03/2025

Kumakhara ndichikhulupililo nthawi zonse amadziwa ndani kuti lelo kungacheso mwantendele?

Athu ambili timakhala ndi mtima opanda chimbekezo pakati tikukhala nmoyo ovuta pazomwe timakumanazo sikuti ziziiwala kuti kunjakuno kuli mulungu

Tonse timakumana ndimavuto ndipo ena oposa nskhu zomwe sitingakwanitse kupilila komatu sikuti sitingakwanitse kupilila ngakhale kuti ndizovuta

Chitsanzo pomwe mulipachibwezi chodzakwatilana ntsongolo pamakhala mayeselo ambili kufikila mutadzakwatilana baibulo limati amene ali ndiwufulu ogonana ndi okhawo akwatilana mwa ambuye zomwe zikusonyeza kuti ngakhale mutatha zaka 20 simungagonane malo amodzi ilo palokha ndiyeso chifukwa pamibado yathu ino izo zachuluka kufusila mkazi lelo mawa kugonana zomwe ndizosenphana ndizomwe baibulo limanena mwachidula masiku ano tatailila taiwala mulungu

Nde sikuti tizingochimwabe ai tikuyenela kudzivomeleza pachomwe tili pomulola mulungu atilowelele nmoyomwathu

Address

125pg Www. Alexsaylet . Com
Dedza

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Promoting independent living . Kulimbikitsa kukhala ndi moyo wodziimila. posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Shortcuts

Share